Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 32:24 - Buku Lopatulika

24 Dzimangireni mizinda ya ana anu, ndi makola a zoweta zanu; ndipo muzichite zotuluka m'kamwa mwanu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

24 Dzimangireni midzi ya ana anu, ndi makola a zoweta zanu; ndipo muzichite zotuluka m'kamwa mwanu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

24 Mangani mizinda ya ana anu, ndi makola a nkhosa zanu, koma muchitedi zimene mwalonjeza.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

24 Amangireni akazi ndi ana anu mizinda, mangani makola a ziweto zanu, koma chitani zomwe mwalonjeza.”

Onani mutuwo Koperani




Numeri 32:24
5 Mawu Ofanana  

Isakara ndiye bulu wolimba, alinkugona pakati pa makola.


Munthu akachitira Yehova chowinda, kapena akalumbira lumbiro ndi kumangira moyo wake chodziletsa, asaipse mau ake; azichita monga mwa zonse zotuluka m'kamwa mwake.


Ndipo anayandikiza, nati Tidzamangira zoweta zathu makola kuno, ndi ana athu mizinda;


Ndipo ana a Gadi ndi ana a Rubeni ananena ndi Mose, nati, Anyamata anu adzachita monga mbuyanga alamulira.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa