Numeri 32:20 - Buku Lopatulika20 Ndipo Mose anati nao, Ngati mudzachita ichi, ndi kudzikonza kunkhondo pamaso pa Yehova, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 Ndipo Mose anati nao, Ngati mudzachita ichi, ndi kudzikonza kunkhondo pamaso pa Yehova, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 Choncho Mose adauza anthuwo kuti, “Muchite izi: mutenge zida pamaso pa Chauta ndi kupita ku nkhondo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 Tsono Mose anati kwa anthuwo, “Ngati inu mudzachita zimenezi, kutenga zida zankhondo pamaso pa Yehova kuti muchite nkhondo, Onani mutuwo |