Numeri 32:19 - Buku Lopatulika19 Pakuti sitidzalandira pamodzi nao tsidya la Yordani, ndi m'tsogolo mwake; popeza cholowa chathu tachilandira tsidya lino la Yordani kum'mawa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 Pakuti sitidzalandira pamodzi nao tsidya la Yordani, ndi m'tsogolo mwake; popeza cholowa chathu tachilandira tsidya lino la Yordani kum'mawa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 Ife ndiye sitidzalandira nao choloŵa chathu patsidya pa Yordanipo kapena patsogolo pake, chifukwa choti talandira choloŵa chathu tsidya lino la Yordani, kuvuma kuno.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 Sitidzalandira cholowa chilichonse pamodzi nawo ku tsidya lina la Yorodani, chifukwa cholowa chathu tachipezera ku tsidya lino la kummawa kwa Yorodani.” Onani mutuwo |