Numeri 32:21 - Buku Lopatulika21 ndi kuoloka Yordani pamaso pa Yehova okonzeka onse mwa inu, kufikira atapirikitsa adani ake pamaso pake, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201421 ndi kuoloka Yordani pamaso pa Yehova okonzeka onse mwa inu, kufikira atapirikitsa adani ake pamaso pake, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa21 Aliyense mwa inu atenge zida, ndipo aoloke mtsinje wa Yordani pamaso pa Chauta ndi kupirikitsa adani ake patsogolo pake, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero21 ndipo ngati nonsenu mudzapita ndi zida kuwoloka Yorodani pamaso pa Yehova mpaka atachotsa adani ake pamaso pake, Onani mutuwo |