Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 32:17 - Buku Lopatulika

17 koma ife tidzakhala okonzeka ndi kufulumira pamaso pa ana a Israele, kufikira tidawafikitsa kumalo kwao; ndi ang'ono athu adzakhala mizinda ya malinga chifukwa cha okhala m'dzikomo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

17 koma ife tidzakhala okonzeka ndi kufulumira pamaso pa ana a Israele, kufikira tidawafikitsa kumalo kwao; ndi ang'ono athu adzakhala m'midzi ya malinga chifukwa cha okhala m'dzikomo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

17 Pambuyo pake tidzatenga zida zankhondo ndi kutsogolera Aisraele mpaka titakaŵafikitsa ku malo ao. Koma ana athu adzakhala m'mizinda yamalinga, chifukwa choopa anthu a m'dziko muno.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

17 Koma ndife okonzeka kutenga zida za nkhondo ndi kupita pamodzi ndi Aisraeli mpaka titakawafikitsa ku malo awo. Panopa, akazi ndi ana athu akhala mʼmizinda yotetezedwa, kuwateteza kwa anthu okhala mʼdzikoli.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 32:17
4 Mawu Ofanana  

Ndipo anayandikiza, nati Tidzamangira zoweta zathu makola kuno, ndi ana athu mizinda;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa