Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 32:10 - Buku Lopatulika

10 Ndipo Yehova anapsa mtima tsiku lija, nalumbira Iye, nati,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

10 Ndipo Yehova anapsa mtima tsiku lija, nalumbira Iye, nati,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

10 Tsono pa tsiku limenelo Chauta adapsa mtima, ndipo adalumbira kuti,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

10 Yehova anakwiya tsiku limenelo ndipo analumbira kuti,

Onani mutuwo Koperani




Numeri 32:10
8 Mawu Ofanana  

Chifukwa chake ndinalumbira mu mkwiyo wanga, ngati adzalowa mpumulo wanga.


Ndipo ndinawakwezeranso dzanja langa m'chipululu, kusawalowetsa m'dzikolo ndidawapatsa, moyenda mkaka ndi uchi, ndilo lokometsetsa mwa maiko onse;


Ndipo Yehova anati kwa Mose, Anthu awa adzaleka liti kundinyoza? Ndipo adzayamba liti kundikhulupirira, chinkana zizindikiro zonse ndinazichita pakati pao?


koma ndithu, pali Ine, dziko lonse lapansi lidzadzazidwa ndi ulemerero wa Yehova;


sadzaona dzikoli ndidalumbirira makolo ao, ngakhale mmodzi wa iwo akundinyoza Ine, sadzaliona;


mitembo yanu idzagwa m'chipululu muno; ndi owerengedwa anu onse, monga mwa kuwerenga kwani konse, kuyambira a zaka makumi awiri ndi mphambu, akudandaula pa Ine;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa