Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Numeri 32:10 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

10 Yehova anakwiya tsiku limenelo ndipo analumbira kuti,

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

10 Ndipo Yehova anapsa mtima tsiku lija, nalumbira Iye, nati,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

10 Ndipo Yehova anapsa mtima tsiku lija, nalumbira Iye, nati,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

10 Tsono pa tsiku limenelo Chauta adapsa mtima, ndipo adalumbira kuti,

Onani mutuwo Koperani




Numeri 32:10
8 Mawu Ofanana  

Choncho ndili chikwiyire, ndinalumbira kuti, “Iwowa sadzalowa ku malo anga a mpumulo.”


Ndinalumbiranso kwa iwo mʼchipululu muja, nditakweza dzanja, kuti sindidzawalowetsanso mʼdziko limene ndinawapatsa, dziko la mwana alirenji, lokoma kwambiri kuposa mayiko ena onse.


Yehova anawuza Mose kuti, “Anthu awa adzandinyoza mpaka liti? Sadzandikhulupirira mpaka liti, ngakhale ndachita zizindikiro zozizwitsa zonsezi pakati pawo?


Komabe, ndikunenetsa kuti pali Ine, ndiponso pamene dziko lapansi ladzaza ndi ulemerero wa Yehova,


palibe ndi mmodzi yemwe wa anthu amenewa amene adzaone dziko limene ndinalonjeza ndi lumbiro kwa makolo awo. Aliyense amene anandinyoza sadzaliona dzikolo.


Mitembo yanu idzakhala ili ngundangunda mʼchipululu muno; mtembo wa munthu aliyense pakati panu amene ali ndi zaka makumi awiri kapena kupitirirapo, amene anawerengedwa pa chiwerengero chija ndipo anangʼungʼudza motsutsana nane.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa