Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 31:42 - Buku Lopatulika

42 Ndipo kunena za gawo la ana a Israele, limene Mose adalichotsa kwa anthu ochita nkhondowo,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

42 Ndipo kunena za gawo la ana a Israele, limene Mose adalichotsa kwa anthu ochita nkhondowo,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

42 Mose adagaŵa zofunkha napatsa Aisraele theka limodzi, kuchotsa pa zofunkha zonse zobwera ndi ankhondo aja.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

42 Pa gawo la Aisraeli, Mose anapatula theka limodzi kuchotsa pa zolanda ku nkhondo zonse zimene zinabwera ndi ankhondo aja.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 31:42
2 Mawu Ofanana  

Ndipo Mose anapereka zamsonkhozo, ndizo nsembe yokweza ya Yehova, kwa Eleazara wansembe, monga Yehova adamuuza Mose.


(ndipo gawo la khamulo ndilo nkhosa zikwi mazana atatu mphambu makumi atatu kudza zisanu ndi ziwiri mphambu mazana asanu,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa