Numeri 31:41 - Buku Lopatulika41 Ndipo Mose anapereka zamsonkhozo, ndizo nsembe yokweza ya Yehova, kwa Eleazara wansembe, monga Yehova adamuuza Mose. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201441 Ndipo Mose anapereka zamsonkhozo, ndizo nsembe yokweza ya Yehova, kwa Eleazara wansembe, monga Yehova adamuuza Mose. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa41 Mose adapereka kwa wansembe Eleazara gawo limene linali loyenera kulipereka kwa Chauta, monga momwe Chauta adaalamulira Moseyo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero41 Mose anapereka kwa wansembe Eliezara gawo limene linali loyenera kupereka kwa Yehova monga momwe Yehova analamulira Mose. Onani mutuwo |