Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 31:40 - Buku Lopatulika

40 Ndipo anthu anafikira zikwi khumi ndi zisanu ndi chimodzi; pamenepo msonkho wa Yehova ndiwo anthu makumi atatu mphambu awiri.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

40 Ndipo anthu anafikira zikwi khumi ndi zisanu ndi chimodzi; pamenepo msonkho wa Yehova ndiwo anthu makumi atatu mphambu awiri.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

40 Anthu analipo 16,000, ndipo 32 anali gawo la Chauta.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

40 anthu analipo 16,000 ndipo gawo la Yehova linali 32.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 31:40
3 Mawu Ofanana  

Ndipo Reu anakhala ndi moyo zaka makumi atatu kudza ziwiri, nabala Serugi:


Ndipo abulu anafikira zikwi makumi atatu ndi mazana asanu; pamenepo msonkho wa Yehova ndiwo makumi asanu ndi limodzi mphambu mmodzi.


Ndipo Mose anapereka zamsonkhozo, ndizo nsembe yokweza ya Yehova, kwa Eleazara wansembe, monga Yehova adamuuza Mose.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa