Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 31:43 - Buku Lopatulika

43 (ndipo gawo la khamulo ndilo nkhosa zikwi mazana atatu mphambu makumi atatu kudza zisanu ndi ziwiri mphambu mazana asanu,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

43 (ndipo gawo la khamulo ndilo nkhosa zikwi mazana atatu mphambu makumi atatu kudza zisanu ndi ziwiri mphambu mazana asanu,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

43 Tsono gawo la Aisraele linali ili: nkhosa 337,500,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

43 Tsono gawo la Aisraeli linali ili: nkhosa 337,500,

Onani mutuwo Koperani




Numeri 31:43
2 Mawu Ofanana  

Ndipo kunena za gawo la ana a Israele, limene Mose adalichotsa kwa anthu ochita nkhondowo,


ndi ng'ombe zikwi makumi atatu mphambu zisanu ndi chimodzi,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa