Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 31:36 - Buku Lopatulika

36 Ndipo limodzi la magawo awiri, ndilo gawo la iwo adatuluka kunkhondo, linafikira nkhosa zikwi mazana atatu mphambu makumi atatu kudza zisanu ndi ziwiri mphambu mazana asanu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

36 Ndipo limodzi la magawo awiri, ndilo gawo la iwo adatuluka kunkhondo, linafikira nkhosa zikwi mazana atatu mphambu makumi atatu kudza zisanu ndi ziwiri mphambu mazana asanu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

36 Gawo la ankhondo amene adapita ku nkhondo linali nkhosa 337,500,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

36 Gawo la ankhondo amene anapita ku nkhondo linali: nkhosa 337,500,

Onani mutuwo Koperani




Numeri 31:36
2 Mawu Ofanana  

ndi anthu, ndiwo akazi osadziwa mwamuna mogona naye, onse pamodzi zikwi makumi atatu ndi ziwiri.


Ndi msonkho wa Yehova wankhosa ndiwo mazana asanu ndi limodzi mphambu makumi asanu ndi awiri mphambu zisanu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa