Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Numeri 31:35 - Buku Lopatulika

35 ndi anthu, ndiwo akazi osadziwa mwamuna mogona naye, onse pamodzi zikwi makumi atatu ndi ziwiri.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

35 ndi anthu, ndiwo akazi osadziwa mwamuna mogona naye, onse pamodzi zikwi makumi atatu ndi ziwiri.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

35 ndi atsikana amene sadagonepo ndi amuna 32,000 pamodzi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

35 ndi atsikana omwe sanagonepo ndi mwamuna 32,000.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 31:35
4 Mawu Ofanana  

Ndipo analanda zoweta zao, ngamira zao zikwi makumi asanu, ndi nkhosa zikwi mazana awiri ndi makumi asanu, ndi abulu zikwi ziwiri, ndi amuna zikwi zana limodzi.


ndi abulu zikwi makumi asanu ndi limodzi mphambu chimodzi,


Ndipo limodzi la magawo awiri, ndilo gawo la iwo adatuluka kunkhondo, linafikira nkhosa zikwi mazana atatu mphambu makumi atatu kudza zisanu ndi ziwiri mphambu mazana asanu.


Koma akazi ndi ana ndi ng'ombe ndi zonse zili m'mzindamo, zankhondo zake zonse, mudzifunkhire nokha; ndipo mudye zankhondo za adani anu, zimene Yehova Mulungu wanu anakupatsani.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa