Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Numeri 31:37 - Buku Lopatulika

37 Ndi msonkho wa Yehova wankhosa ndiwo mazana asanu ndi limodzi mphambu makumi asanu ndi awiri mphambu zisanu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

37 Ndi msonkho wa Yehova wankhosa ndiwo mazana asanu ndi limodzi mphambu makumi asanu ndi awiri mphambu zisanu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

37 ndipo gawo la Chauta linali nkhosa 675.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

37 mwa zimenezi gawo la Yehova linali 675;

Onani mutuwo Koperani




Numeri 31:37
3 Mawu Ofanana  

Ndipo limodzi la magawo awiri, ndilo gawo la iwo adatuluka kunkhondo, linafikira nkhosa zikwi mazana atatu mphambu makumi atatu kudza zisanu ndi ziwiri mphambu mazana asanu.


Ndipo ng'ombe zidafikira zikwi makumi atatu mphambu zisanu ndi chimodzi; pamenepo msonkho wa Yehova ndiwo makumi asanu ndi awiri mphambu ziwiri.


Ndipo muchitire Yehova Mulungu wanu chikondwerero cha Masabata, ndiwo msonkho waufulu wa dzanja lanu, umene mupereke monga Yehova Mulungu wanu akudalitsani.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa