Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 31:19 - Buku Lopatulika

19 Ndipo mukhale m'misasa kunja kwa chigono masiku asanu ndi awiri; aliyense adapha munthu, ndi aliyense wakukhudza wophedwa, mudziyeretse tsiku lachitatu ndi lachisanu ndi chiwiri, inu ndi andende anu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

19 Ndipo mukhale m'misasa kunja kwa chigono masiku asanu ndi awiri; aliyense adapha munthu, ndi aliyense wakukhudza wophedwa, mudziyeretse tsiku lachitatu ndi lachisanu ndi chiwiri, inu ndi andende anu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

19 Tsono aliyense mwa inu amene wapha munthu, kapena amene wakhudza mtembo, akhale kunja kwa mahema masiku asanu ndi aŵiri. Pa tsiku lachitatu ndi pa tsiku lachisanu ndi chiŵiri, mudziyeretse inuyo pamodzi ndi akapolo anu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

19 “Inu nonse amene mwaphapo wina wake, kapena kukhudza aliyense amene anaphedwa mukhale kunja kwa msasa masiku asanu ndi awiri. Pa tsiku lachitatu mudziyeretse nokha pamodzi ndi akapolo anu.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 31:19
5 Mawu Ofanana  

Koma mau a Yehova anandidzera, kuti, Wakhetsa mwazi wochuluka, popeza wachita nkhondo zazikulu; sudzamangira dzina langa nyumba, popeza wakhetsa pansi mwazi wambiri pamaso panga;


Koma ana aakazi onse osadziwa mwamuna mogona naye, asungeni ndi moyo akhale anu.


Muyeretse zovala zanu zonse, zipangizo zonse zachikopa, ndi zoomba zonse za ubweya wa mbuzi, ndi zipangizo zonse za mtengo.


Uza ana a Israele kuti azitulutsa m'chigono akhate onse, ndi onse akukhala nako kukha, ndi onse odetsedwa chifukwa cha akufa;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa