Numeri 31:18 - Buku Lopatulika18 Koma ana aakazi onse osadziwa mwamuna mogona naye, asungeni ndi moyo akhale anu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Koma ana akazi onse osadziwa mwamuna mogona naye, asungeni ndi moyo akhale anu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Koma atsikana amene sadagone ndi mwamuna, muŵasunge akhale anu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 koma sungani mtsikana aliyense amene sanagonepo ndi mwamuna. Onani mutuwo |