Numeri 31:17 - Buku Lopatulika17 Ndipo tsono iphani amuna onse mwa anawo, iphaninso akazi onse akudziwa mwamuna mogona naye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Ndipo tsono iphani amuna onse mwa anawo, iphaninso akazi onse akudziwa mwamuna mogona naye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Nchifukwa chake tsono iphani mwana wamwamuna aliyense, ndi mkazi aliyense amene adadziŵapo ndi mwamuna. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Tsopano iphani munthu wamwamuna aliyense. Ndiponso iphani mayi aliyense amene anagonapo ndi mwamuna, Onani mutuwo |