Numeri 31:15 - Buku Lopatulika15 Ndipo Mose ananena nao, Kodi mwasunga ndi moyo akazi onse? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Ndipo Mose ananena nao, Kodi mwasunga ndi moyo akazi onse? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Mose adaŵafunsa kuti, “Chifukwa chiyani mwaŵasiya amoyo akazi onse? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 Iye anafunsa kuti, “Kodi nʼchifukwa chiyani mwawaleka amoyo amayi onsewa?” Onani mutuwo |