Numeri 30:3 - Buku Lopatulika3 Ndipo mkazi akachitira Yehova chowinda, nakadzimanga nacho chodziletsa, pokhala ali m'nyumba ya atate wake, mu unamwali; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Ndipo mkazi akachitira Yehova chowinda, nakadzimanga nacho chodziletsa, pokhala ali m'nyumba ya atate wake, m'unamwali; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Mkazi akakhala mtsikana, nakhalabe m'nyumba ya bambo wake, ndipo alumbira kwa Chauta kuti adzachitadi zina zake zimene walumbira, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 “Pamene munthu wamkazi amene akukhalabe mʼnyumba ya abambo ake alumbira kwa Yehova kuti adzachita zimene walonjeza pa ubwana wake, Onani mutuwo |