Numeri 30:3 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 “Pamene munthu wamkazi amene akukhalabe mʼnyumba ya abambo ake alumbira kwa Yehova kuti adzachita zimene walonjeza pa ubwana wake, Onani mutuwoBuku Lopatulika3 Ndipo mkazi akachitira Yehova chowinda, nakadzimanga nacho chodziletsa, pokhala ali m'nyumba ya atate wake, mu unamwali; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Ndipo mkazi akachitira Yehova chowinda, nakadzimanga nacho chodziletsa, pokhala ali m'nyumba ya atate wake, m'unamwali; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Mkazi akakhala mtsikana, nakhalabe m'nyumba ya bambo wake, ndipo alumbira kwa Chauta kuti adzachitadi zina zake zimene walumbira, Onani mutuwo |