Numeri 30:15 - Buku Lopatulika15 Koma akazifafaniza atatha kuzimva; pamenepo adzasenza mphulupulu yake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Koma akazifafaniza atatha kuzimva; pamenepo adzasenza mphulupulu yake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Koma mwamunayo akamkaniza patapita kanthaŵi atazimva kale, iyeyo ndiye wochimwa pamalo pa mkaziyo.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 Koma ngati mwamunayo amukaniza patapita kanthawi atazimva kale, iyeyo ndiye wochimwa mʼmalo mwa mayiyo.” Onani mutuwo |