Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 30:16 - Buku Lopatulika

16 Awa ndi malemba amene Yehova analamulira Mose, a pakati pa mwamuna ndi mkazi wake, pakati pa atate ndi mwana wake wamkazi, akali namwali, m'nyumba ya atate wake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

16 Awa ndi malemba amene Yehova analamulira Mose, a pakati pa mwamuna ndi mkazi wake, pakati pa atate ndi mwana wake wamkazi, akali namwali, m'nyumba ya atate wake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

16 Ameneŵa ndiwo malamulo amene Chauta adalamula Mose za mwamuna ndi mkazi wake, ndiponso za bambo ndi mwana wake wamkazi amene akadali mtsikana wokhalabe m'nyumba ya bambo wake.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

16 Awa ndiwo malamulo amene Yehova analamula Mose za mwamuna ndi mkazi wake, ndiponso abambo ndi mwana wawo wamkazi amene akanali mtsikana wokhalabe mʼnyumba ya abambo akewo.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 30:16
7 Mawu Ofanana  

Ichi ndi chilamulo cha nthenda yakhate ili pa chovala chaubweya kapena chathonje, ngakhale pamuyaro, kapena pamtsendero, kapena pa chinthu chilichonse chopangika ndi chikopa; kuchitcha choyera kapena kuchitcha chodetsa.


Koma akazifafaniza atatha kuzimva; pamenepo adzasenza mphulupulu yake.


Ndipo Yehova ananena ndi Mose, nati,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa