Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 30:11 - Buku Lopatulika

11 ndipo mwamuna wake anamva, koma anakhala naye chete osamletsa, pamenepo zowinda zake zonse zidzakhazikika, ndi zodziletsa zonse anamanga nazo moyo wake zidzakhazikika.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

11 ndipo mwamuna wake anamva, koma anakhala naye chete osamletsa, pamenepo zowinda zake zonse zidzakhazikika, ndi zodziletsa zonse anamanga nazo moyo wake zidzakhazikika.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

11 tsono mwamuna wake nkumva, koma osamuuza kanthu mkaziyo ndiponso osamkaniza, ayenera kuchitadi zonse zimene adalumbira ndi zonse zimene adalonjeza.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

11 mwamuna wake ndi kumva kulumbira kwakeko koma osayankhulapo kanthu, osamuletsa, ayenera kuchitadi zonse zimene walumbira ndi zonse zimene walonjeza.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 30:11
3 Mawu Ofanana  

Ndipo ngati anawinda m'nyumba ya mwamuna wake, kapena anamanga moyo wake ndi chodziletsa ndi kulumbirapo,


Koma ngati mwamuna wake anazifafanizadi tsiku lakuzimva iye, zonse zotuluka m'milomo yake kunena za zowinda zake, kapena za chodziletsa cha moyo wake sizidzakhazikika; mwamuna wake anafafaniza; ndipo Yehova adzamkhululukira iye.


Koma atate wake akamletsa tsiku lakumva iye; zowinda zake zonse, ndi zodziletsa zake zonse anamanga nazo moyo wake, sizidzakhazikika; ndipo Yehova adzamkhululukira, popeza atate wake anamletsa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa