Numeri 30:10 - Buku Lopatulika10 Ndipo ngati anawinda m'nyumba ya mwamuna wake, kapena anamanga moyo wake ndi chodziletsa ndi kulumbirapo, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Ndipo ngati anawinda m'nyumba ya mwamuna wake, kapena anamanga moyo wake ndi chodziletsa ndi kulumbirapo, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 “Mkazi wokwatiwa akalonjeza nalumbira kuti adzachitadi zimene walonjeza, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 “Koma ngati mayi wokwatiwa alumbira nalonjeza kuti adzachitadi zimene walonjeza, Onani mutuwo |