Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 30:1 - Buku Lopatulika

1 Ndipo Mose ananena ndi akulu a mafuko a ana a Israele, nati, Chinthu anachilamulira Yehova ndi ichi:

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

1 Ndipo Mose ananena ndi akulu a mafuko a ana a Israele, nati, Chinthu anachilamulira Yehova ndi ichi:

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

1 Mose adauza atsogoleri a mafuko a Aisraele kuti, Chauta walamula kuti,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

1 Mose anawuza Aisraeli onse zonse zimene Yehova anamulamula. Iye anati, “Zimene Yehova walamula ndi izi:

Onani mutuwo Koperani




Numeri 30:1
8 Mawu Ofanana  

Ndipo Mose anasankha amuna anzeru mwa Aisraele onse, nawaika akulu a pa anthu, akulu a pa zikwi, akulu a pa mazana, akulu a pa makumi asanu, ndi akulu a pa makumi.


Ndipo Mose anauza Aroni mau onse a Yehova amene adamtuma nao, ndi zizindikiro zonse zimene adamlamulira.


Ndipo Mose ananena ndi ana a Israele monga mwa zonse Yehova adamuuza Mose.


akalonga a Israele, akulu a nyumba za makolo ao, anapereka nsembe, ndiwo akalonga a mafuko akuyang'anira owerengedwa;


Mukawindira Yehova Mulungu wanu chowinda, musamachedwa kuchichita; popeza Yehova Mulungu wanu adzakufunsani za ichi ndithu ndipo mukadachimwako.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa