Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Numeri 30:1 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

1 Mose anawuza Aisraeli onse zonse zimene Yehova anamulamula. Iye anati, “Zimene Yehova walamula ndi izi:

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

1 Ndipo Mose ananena ndi akulu a mafuko a ana a Israele, nati, Chinthu anachilamulira Yehova ndi ichi:

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

1 Ndipo Mose ananena ndi akulu a mafuko a ana a Israele, nati, Chinthu anachilamulira Yehova ndi ichi:

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

1 Mose adauza atsogoleri a mafuko a Aisraele kuti, Chauta walamula kuti,

Onani mutuwo Koperani




Numeri 30:1
8 Mawu Ofanana  

Iye anasankha amuna odziwa bwino ntchito zawo ndipo anawayika kuti akhale atsogoleri, oyangʼanira anthu motere: atsogoleri a anthu 1,000, ena a anthu 500, ena a anthu makumi asanu ndi ena a anthu khumi.


Kenaka Mose anamufotokozera Aaroni chilichonse chimene Yehova anamutuma kuti akanene. Anamufotokozera za zizindikiro zozizwitsa zimene anamulamulira kuti akazichite.


Mose anawuza Aisraeli zonse zimene Yehova anamulamulira.


Kenaka atsogoleri a Aisraeli, akuluakulu a mabanja omwe ankayangʼanira mafuko a anthu omwe anawawerenga aja, anachita chopereka.


Mukalumbira kupereka kanthu kwa Yehova Mulungu wanu, musamachedwetse kupereka, chifukwa Yehova Mulungu wanu adzakufunsanibe kanthuko ndipo mudzapezeka wochimwa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa