Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 29:40 - Buku Lopatulika

40 Ndipo Mose ananena ndi ana a Israele monga mwa zonse Yehova adamuuza Mose.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

40 Ndipo Mose ananena ndi ana a Israele monga mwa zonse Yehova adamuuza Mose.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

40 Tsono Mose adauza Aisraele zonse, monga momwe Chauta adaamlamulira.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

40 Mose anawuza Aisraeli zonse zimene Yehova anamulamulira.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 29:40
9 Mawu Ofanana  

Anatero Mose; monga mwa zonse Yehova adamuuza, momwemo anachita.


Izi muzikonzera Yehova mu zikondwerero zanu zoikika, pamodzi ndi zowinda zanu, ndi zopereka zanu zaufulu, za nsembe zanu zopsereza, ndi za nsembe zanu zaufa, ndi za nsembe zanu zothira, ndi za nsembe zanu zoyamika.


Ndipo Mose ananena ndi akulu a mafuko a ana a Israele, nati, Chinthu anachilamulira Yehova ndi ichi:


ndi kuwaphunzitsa, asunge zinthu zonse zimene ndinakulamulani inu; ndipo onani, Ine ndili pamodzi ndi inu masiku onse, kufikira chimaliziro cha nthawi ya pansi pano.


Pakuti sindinakubisirani pakukulalikirani uphungu wonse wa Mulungu.


Pakuti ndinapereka kwa inu poyamba, chimenenso ndinalandira, kuti Khristu anafera zoipa zathu, monga mwa malembo;


Taonani, ndinakuphunzitsani malemba ndi maweruzo, monga Yehova Mulungu wanga anandiuza ine, kuti muzichita chotero pakati padziko limene munkako kulilandira likhale lanulanu.


amene anakhala wokhulupirika kwa Iye adamuikayo, monganso Mose m'nyumba yake yonse.


Ndipo Mosetu anali wokhulupirika m'nyumba yake yonse, monga mnyamata, achitire umboni izi zidzalankhulidwazi;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa