Numeri 3:7 - Buku Lopatulika7 Ndipo azisunga udikiro wake, ndi udikiro wa khamu lonse pa khomo la chihema chokomanako, kuchita ntchito ya Kachisi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Ndipo azisunga udikiro wake, ndi udikiro wa khamu lonse pa khomo la chihema chokomanako, kuchita ntchito ya Kachisi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Azigwirira ntchito iyeyo ndi mpingo wonse, pakhomo pa chihema chamsonkhano, monga momwe amachitira potumikira m'Chihema cha Mulungu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Azigwira ntchito yothandiza iyeyo ndi gulu lonse ku tenti ya msonkhano pogwira ntchito ya ku Chihema. Onani mutuwo |