Numeri 3:6 - Buku Lopatulika6 Sendera nalo kuno fuko la Levi, ndi kuwaika pamaso pa Aroni wansembe, kuti amtumikire. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Sendera nalo kuno fuko la Levi, ndi kuwaika pamaso pa Aroni wansembe, kuti amtumikire. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 “Bwera nawo anthu a fuko la Levi, ndipo uŵapereke kwa wansembe Aroni kuti azimtumikira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 “Bweretsa fuko la Levi ndipo ulipereke kwa Aaroni wansembe kuti lizimutumikira. Onani mutuwo |