Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 3:42 - Buku Lopatulika

42 Ndipo Mose anawawerenga, monga Yehova adamuuza, oyamba kubadwa onse mwa ana a Israele.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

42 Ndipo Mose anawawerenga, monga Yehova adamuuza, oyamba kubadwa onse mwa ana a Israele.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

42 Choncho Mose adaŵerenga ana onse achisamba, monga Chauta adamlamula.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

42 Choncho Mose anawerenga ana aamuna onse oyamba kubadwa a Aisraeli monga momwe Yehova anamulamulira.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 3:42
2 Mawu Ofanana  

Ndipo unditengere Ine Alevi (Ine ndine Yehova) m'malo mwa oyamba kubadwa onse mwa ana a Israele; ndi ng'ombe za Alevi m'malo mwa zoyamba kubadwa zonse mwa ng'ombe za ana a Israele.


Ndipo amuna onse oyamba kubadwa, powerenga maina, kuyambira a mwezi umodzi ndi mphambu, owerengedwa ao, ndiwo zikwi makumi awiri mphambu ziwiri kudza mazana awiri ndi makumi asanu ndi awiri mphambu atatu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa