Numeri 3:20 - Buku Lopatulika20 Ndi ana a Merari monga mwa mabanja ao: Mali ndi Musi. Awa ndi mabanja a Alevi monga mwa nyumba za makolo ao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 Ndi ana a Merari monga mwa mabanja ao: Mali ndi Musi. Awa ndi mabanja a Alevi monga mwa nyumba za makolo ao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 Ndipo ana a Merari potsata mabanja ao ndi aŵa: Mali ndi Musi. Ameneŵa ndiwo mabanja a Levi potsata banja la makolo ao. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 Ana a Merari potsata mabanja awo ndi awa: Mali ndi Musi. Amenewa ndiwo anali mabanja a Alevi monga mwa makolo awo. Onani mutuwo |