Numeri 3:10 - Buku Lopatulika10 Koma uike Aroni ndi ana ake aamuna, azisunga ntchito yao ya nsembe; ndi mlendo wakusendera pafupi amuphe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Koma uike Aroni ndi ana ake amuna, azisunga ntchito yao ya nsembe; ndi mlendo wakusendera pafupi amuphe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Umusankhe Aroni ndi ana ake, kuti azitumikira pa ntchito yaunsembe. Koma wina aliyense akayandikira pafupi, aphedwe.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Usankhe Aaroni ndi ana ake aamuna kuti azitumikira pa ntchito ya unsembe. Koma wina aliyense woyandikira malo opatulika aphedwe.” Onani mutuwo |