Numeri 3:10 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Usankhe Aaroni ndi ana ake aamuna kuti azitumikira pa ntchito ya unsembe. Koma wina aliyense woyandikira malo opatulika aphedwe.” Onani mutuwoBuku Lopatulika10 Koma uike Aroni ndi ana ake aamuna, azisunga ntchito yao ya nsembe; ndi mlendo wakusendera pafupi amuphe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Koma uike Aroni ndi ana ake amuna, azisunga ntchito yao ya nsembe; ndi mlendo wakusendera pafupi amuphe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Umusankhe Aroni ndi ana ake, kuti azitumikira pa ntchito yaunsembe. Koma wina aliyense akayandikira pafupi, aphedwe.” Onani mutuwo |