Numeri 29:6 - Buku Lopatulika6 pamodzi ndi nsembe yopsereza ya pamwezi, ndi nsembe yake yaufa, ndi nsembe yopsereza yosalekeza, ndi nsembe yake yaufa, ndi nsembe zake zothira, monga mwa lemba lake, zikhale za fungo lokoma, nsembe yamoto ya Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 pamodzi ndi nsembe yopsereza ya pamwezi, ndi nsembe yake yaufa, ndi nsembe yopsereza yosalekeza, ndi nsembe yake yaufa, ndi nsembe zake zothira, monga mwa lemba lake, zikhale za fungo lokoma, nsembe yamoto ya Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Mupereke zonsezi kuwonjezera pa nsembe yopsereza yopereka mwezi ukakhala, pamodzi ndi chopereka chake cha chakudya, kuwonjezeranso pa nsembe zopsereza za tsiku ndi tsiku zija, pamodzi ndi nsembe zaufa ndi zopereka za chakumwa, potsata malamulo ake, kuti zitulutse fungo lokoma, nsembe zotentha pa moto, zopereka kwa Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Izi ndi zowonjezera pa nsembe zopsereza za mwezi ndi mwezi komanso za tsiku ndi tsiku pamodzi ndi zopereka za chakudya ndi zopereka za chakumwa potsata malamulo ake. Izi ndi zopereka zotentha pa moto, zoperekedwa kwa Yehova, fungo lokoma. Onani mutuwo |