Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 29:5 - Buku Lopatulika

5 ndi tonde mmodzi wa nsembe yauchimo, yakutetezera inu;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

5 ndi tonde mmodzi wa nsembe yauchimo, yakutetezera inu;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

5 Muperekenso tonde mmodzi kuti akhale nsembe yochitira mwambo wopepesera machimo anu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

5 Muziperekanso mbuzi yayimuna kuti izikhala nsembe yopepesera machimo anu.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 29:5
6 Mawu Ofanana  

Ndipo anatenga malaya ake a Yosefe, napha tonde, naviika malaya m'mwazi wake:


Ndi tonde mmodzi, akhale nsembe yauchimo ya Yehova; aikonze pamodzi ndi nsembe yopsereza yosalekeza, ndi nsembe yake yothira.


ndi tonde mmodzi akhale nsembe yauchimo, yakutetezera inu.


tonde mmodzi wakutetezera inu.


ndi limodzi la magawo khumi likhale la mwanawankhosa mmodzi, momwemo ndi anaankhosa asanu ndi awiri;


pamodzi ndi nsembe yopsereza ya pamwezi, ndi nsembe yake yaufa, ndi nsembe yopsereza yosalekeza, ndi nsembe yake yaufa, ndi nsembe zake zothira, monga mwa lemba lake, zikhale za fungo lokoma, nsembe yamoto ya Yehova.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa