Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 29:4 - Buku Lopatulika

4 ndi limodzi la magawo khumi likhale la mwanawankhosa mmodzi, momwemo ndi anaankhosa asanu ndi awiri;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

4 ndi limodzi la magawo khumi likhale la mwanawankhosa mmodzi, momwemo ndi anaankhosa asanu ndi awiri;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

4 ndiponso wa kilogaramu limodzi pa mwanawankhosa aliyense.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

4 Pa mwana wankhosa aliyense mwa asanu ndi awiri aja muzipereka kilogalamu imodzi.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 29:4
2 Mawu Ofanana  

ndi nsembe yao yaufa, ufa wosalala wosakaniza ndi mafuta, atatu a magawo khumi akhale a ng'ombeyo, awiri a magawo khumi akhale a nkhosa yamphongo,


ndi tonde mmodzi wa nsembe yauchimo, yakutetezera inu;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa