Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 29:23 - Buku Lopatulika

23 Ndi tsiku lachinai ng'ombe khumi, nkhosa zamphongo ziwiri, anaankhosa khumi ndi anai, a chaka chimodzi, opanda chilema;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

23 Ndi tsiku lachinai ng'ombe khumi, nkhosa zamphongo ziwiri, anaankhosa khumi ndi anai, a chaka chimodzi, opanda chilema;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

23 “Pa tsiku lachinai mupereke ng'ombe khumi zamphongo, nkhosa ziŵiri zamphongo, anaankhosa amphongo khumi ndi anai a chaka chimodzi opanda chilema,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

23 “ ‘Pa tsiku lachinayi muzipereka ngʼombe zazimuna khumi, nkhosa zazimuna ziwiri ndi ana ankhosa aamuna khumi ndi anayi a chaka chimodzi, zonse zopanda chilema.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 29:23
3 Mawu Ofanana  

ndi tonde mmodzi akhale nsembe yauchimo; pamodzi ndi nsembe yopsereza yosalekeza, ndi nsembe yake yaufa, ndi nsembe yake yothira.


nsembe yake yaufa, ndi nsembe zake zothira za ng'ombe, za nkhosa zamphongo, ndi za anaankhosa, monga mwa kuwerenga kwake, ndi kutsata lemba lake;


Koma pamene padafika pakati pa chikondwerero, Yesu anakwera nalowa mu Kachisi, naphunzitsa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa