Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 29:10 - Buku Lopatulika

10 limodzi la magawo khumi likhale la mwanawankhosa mmodzi, momwemo ndi anaankhosa asanu ndi awiri;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

10 limodzi la magawo khumi likhale la mwanawankhosa mmodzi, momwemo ndi anaankhosa asanu ndi awiri;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

10 ndiponso wa kilogaramu limodzi pa mwanawankhosa aliyense.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

10 kilogalamu imodzi pa mwana wankhosa aliyense mwa asanu ndi awiriwo.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 29:10
3 Mawu Ofanana  

ndi atatu a magawo khumi a efa wa ufa wosalala, ikhale nsembe yaufa, wosakaniza ndi mafuta, ndiwo wa ng'ombe iliyonse; ndi awiri a magawo khumi a ufa wosalala, ikhale nsembe yaufa, wosakaniza ndi mafuta, ndiwo wa nkhosa yamphongo imodziyo;


tonde mmodzi akhale nsembe yauchimo, pamodzi ndi nsembe yauchimo yotetezera, ndi nsembe yopsereza yosalekeza, ndi nsembe yake yaufa, ndi nsembe zake zothira.


ndi nsembe yao ya ufa wosalala wosakaniza ndi mafuta, atatu a magawo khumi akhale a ng'ombe, awiri a magawo khumi akhale a nkhosa yamphongo imodziyo;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa