Numeri 28:25 - Buku Lopatulika25 Ndipo tsiku lachisanu ndi chiwiri mukhale nako kusonkhana kopatulika; musamachita ntchito ya masiku ena. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201425 Ndipo tsiku lachisanu ndi chiwiri mukhale nako kusonkhana kopatulika; musamachita ntchito ya masiku ena. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa25 Ndipo pa tsiku lachisanu ndi chiŵiri muchite msonkhano wopatulika. Musagwire ntchito zotopetsa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero25 Pa tsiku lachisanu ndi chiwiri muzichita msonkhano wopatulika ndipo musamagwire ntchito iliyonse. Onani mutuwo |