Numeri 27:23 - Buku Lopatulika23 namuikira manja ake, namlangiza monga Yehova adanena ndi dzanja la Mose. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201423 namuikira manja ake, namlangiza monga Yehova adanena ndi dzanja la Mose. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa23 Ndipo adamsanjika manja, nampatsa udindo monga momwe Chauta adamlangizira kudzera mwa Mose. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero23 Ndipo anamusanjika manja ndi kumupatsa mphamvu, monga Yehova ananenera kudzera mwa Mose. Onani mutuwo |