Numeri 26:51 - Buku Lopatulika51 Iwo ndiwo owerengedwa ao a ana a Israele, zikwi mazana asanu ndi limodzi mphambu chimodzi kudza mazana asanu ndi awiri mphambu makumi atatu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201451 Iwo ndiwo owerengedwa ao a ana a Israele, zikwi mazana asanu ndi limodzi mphambu chimodzi kudza mazana asanu ndi awiri mphambu makumi atatu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa51 Chiŵerengero chonse cha Aisraele chinali 601,730. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero51 Chiwerengero chonse cha amuna mu Israeli chinalipo 601,730. Onani mutuwo |