Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Numeri 26:51 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

51 Chiwerengero chonse cha amuna mu Israeli chinalipo 601,730.

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

51 Iwo ndiwo owerengedwa ao a ana a Israele, zikwi mazana asanu ndi limodzi mphambu chimodzi kudza mazana asanu ndi awiri mphambu makumi atatu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

51 Iwo ndiwo owerengedwa ao a ana a Israele, zikwi mazana asanu ndi limodzi mphambu chimodzi kudza mazana asanu ndi awiri mphambu makumi atatu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

51 Chiŵerengero chonse cha Aisraele chinali 601,730.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 26:51
11 Mawu Ofanana  

Munachulukitsa ana awo aamuna ngati nyenyezi za mlengalenga. Ndipo munawabweretsa mʼdziko limene munawuza makolo awo kuti alilowe ndi kulitenga.


Chimene Iye wapasula palibe angachimangenso. Akatsekera munthu mʼndende palibe angamutulutse.


Inu munatsogolera anthu anu ngati gulu la nkhosa mwa dzanja la Mose ndi Aaroni.


Aisraeli anayenda ulendo kuchokera ku Ramesesi mpaka kukafika ku Sukoti. Anthu aamuna oyenda pansi analipo 600,000 osawerengera akazi ndi ana.


Munthu aliyense amapereka beka imodzi, kufanana ngati makilogalamu 6, potsata muyeso wa ku malo wopatulika. Kuchokera kwa aliyense amene anawerengedwa kuyambira zaka 20 kapena kuposerapo, amuna onse analipo 603,550.


Chiwerengero cha anthu onse pamodzi chinali 603,550.


Koma Mose anati, “Taonani pano ndili pakati pa anthu 600,000 amene ndi kuyenda nawo ndipo Inuyo mukuti, ‘Ndidzawapatsa nyama kuti adye mwezi wathunthu!’


Amenewa ndi Aisraeli monga mwa mabanja a makolo awo. Chiwerengero cha Aisraeli onse mʼmisasa chinali 603,550, mwa magulu awo.


Yehova anawuza Mose kuti,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa