Numeri 26:43 - Buku Lopatulika43 Mabanja onse a Asuhamu monga mwa owerengedwa ao ndiwo zikwi makumi asanu ndi limodzi mphambu zinai kudza mazana anai. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201443 Mabanja onse a Asuhamu monga mwa owerengedwa ao ndiwo zikwi makumi asanu ndi limodzi mphambu zinai kudza mazana anai. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa43 Anthu oŵerengedwa pa mabanja onse a Suhamu adakwanira 64,400. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero43 Onse a fuko la Asuhamu amene anawerengedwa analipo 64,400. Onani mutuwo |