Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 26:42 - Buku Lopatulika

42 Mwana wamwamuna wa Dani monga mwa mabanja ake ndiye Suhamu, ndiye kholo la banja la Asuhamu. Iwo ndiwo mabanja a Dani monga mwa mabanja ao.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

42 Mwana wamwamuna wa Dani monga mwa mabanja ake ndiye Suhamu, ndiye kholo la banja la Asuhamu. Iwo ndiwo mabanja a Dani monga mwa mabanja ao.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

42 Potsata mabanja ao ana aamuna a Dani anali aŵa: Suhamu anali kholo la banja la Asuhamu. Ameneŵa ndiwo mabanja a Dani potsata mabanja ao.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

42 Zidzukulu za Dani mwa mabanja awo zinali izi: kuchokera mwa Suhamu fuko la Asuhamu. Izi zinali zidzukulu za Dani.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 26:42
4 Mawu Ofanana  

Ndi ana aamuna a Dani: Husimu.


A ana a Dani, kubadwa kwao, monga mwa mabanja ao, monga mwa nyumba za makolo ao, powerenga maina, kuyambira a zaka makumi awiri ndi mphambu, onse akutulukira kunkhondo;


Iwo ndiwo ana a Benjamini monga mwa mabanja ao; ndipo owerengedwa ao ndiwo zikwi makumi anai mphambu zisanu kudza mazana asanu ndi limodzi.


Mabanja onse a Asuhamu monga mwa owerengedwa ao ndiwo zikwi makumi asanu ndi limodzi mphambu zinai kudza mazana anai.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa