Numeri 25:1 - Buku Lopatulika1 Ndipo Israele anakhala mu Sitimu, ndipo anthu anayamba kuchita chigololo ndi ana aakazi a Mowabu; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Ndipo Israele anakhala m'Sitimu, ndipo anthu anayamba kuchita chigololo ndi ana akazi a Mowabu; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Pamene Aisraele anali ku Sitimu, anthu aamuna adayamba kuchita dama ndi akazi a ku Mowabu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Aisraeli akukhala ku Sitimu, anayamba kuchita chigololo ndi akazi a ku Mowabu, Onani mutuwo |