Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 24:25 - Buku Lopatulika

25 Ndipo Balamu anauka, namuka nabwerera kumalo kwake; ndi Balaki yemwe ananka njira yake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

25 Ndipo Balamu anauka, namuka nabwerera kumalo kwake; ndi Balaki yemwe ananka njira yake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

25 Tsono Balamu adanyamuka nabwerera kwao. Balaki nayenso adapita kwao.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

25 Pamenepo Balaamu ananyamuka ndi kubwerera kwawo ndipo Balaki anapitanso njira yake.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 24:25
5 Mawu Ofanana  

Chifukwa chake thawira ku malo ako tsopano; ndikadakuchitira ulemu waukulu; koma, taona, Yehova wakuletsera ulemu.


Ndipo tsopano, taonani, ndimuka kwa anthu a mtundu wanga; tiyeni, ndidzakulangizani, ndi kukuuzani zimene anthu awa adzachitira anthu anu, masiku otsiriza.


Ndipo Israele anakhala mu Sitimu, ndipo anthu anayamba kuchita chigololo ndi ana aakazi a Mowabu;


Ndipo anapha mafumu a Amidiyani pamodzi ndi ophedwa ao ena; ndiwo Evi, ndi Rekemu, ndi Zuri, ndi Huri, ndi Reba, mafumu asanu a Amidiyani; namupha Balamu mwana wa Beori ndi lupanga.


Ana a Israele anaphanso ndi lupanga Balamu mwana wa Beori, mlauli uja, pamodzi ndi ena adawaphawo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa