Numeri 24:25 - Buku Lopatulika25 Ndipo Balamu anauka, namuka nabwerera kumalo kwake; ndi Balaki yemwe ananka njira yake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201425 Ndipo Balamu anauka, namuka nabwerera kumalo kwake; ndi Balaki yemwe ananka njira yake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa25 Tsono Balamu adanyamuka nabwerera kwao. Balaki nayenso adapita kwao. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero25 Pamenepo Balaamu ananyamuka ndi kubwerera kwawo ndipo Balaki anapitanso njira yake. Onani mutuwo |