Numeri 24:16 - Buku Lopatulika16 anenetsa wakumva mau a Mulungu, ndi kudziwa nzeru ya Wam'mwambamwamba, wakuona masomphenya a Wamphamvuyonse, wakugwa pansi wopenyuka maso. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 anenetsa wakumva mau a Mulungu, ndi kudziwa nzeru ya Wam'mwambamwamba, wakuona masomphenya a Wamphamvuyonse, wakugwa pansi wopenyuka maso. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 munthu amene akumva mau a Mulungu, ndipo akudziŵa nzeru zake za Wopambanazonse, munthu amene akuwona Mphambe m'masomphenya, munthu amene akugwa pansi, koma maso ake ali chipenyere. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Uthenga wa amene amamva mawu a Mulungu, amene ali ndi nzeru zochokera kwa Wammwambamwamba, amene amaona masomphenya wochokera kwa Wamphamvuzonse, amene amagwa chafufumimba koma diso lake lili lotsekuka: Onani mutuwo |