Numeri 23:5 - Buku Lopatulika5 Ndipo Yehova anaika mau m'kamwa mwa Balamu, nati, Bwerera kwa Balaki, nukanene chakutichakuti. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Ndipo Yehova anaika mau m'kamwa mwa Balamu, nati, Bwerera kwa Balaki, nukanene chakutichakuti. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Tsono Chauta adauza Balamu kuti “Bwerera kwa Balaki, ukamuuze izi! Izi” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Yehova anawuza Balaamu kuti, “Bwerera kwa Balaki ndipo ukamuwuze uthenga uwu.” Onani mutuwo |