Numeri 23:26 - Buku Lopatulika26 Koma Balamu anayankha nati kwa Balaki, Sindinakuuzani ndi kuti, Chilichonse achinena Yehova, chomwecho ndizichita? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201426 Koma Balamu anayankha nati kwa Balaki, Sindinakuuzani ndi kuti, Chilichonse achinena Yehova, chomwecho ndizichita? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa26 Koma Balamu adafunsa Balakiyo kuti, “Kodi sindidakuuzeni kuti ndiyenera kuchita zonse zimene Chauta wandiwuza?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero26 “Balaamu anayankha Balaki kuti, ‘Kodi sindinakuwuzeni kuti ndiyenera kuchita zimene Yehova wanena?’ ” Onani mutuwo |