Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 23:25 - Buku Lopatulika

25 Ndipo Balaki anati kwa Balamu, Usawatemberera konse, kapena kuwadalitsa konse.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

25 Ndipo Balaki anati kwa Balamu, Usawatemberera konse, kapena kuwadalitsa konse.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

25 Balaki adauza Balamu kuti, “Musaŵatemberere, ndipo musaŵadalitse.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

25 Ndipo Balaki anati kwa Balaamu, “Usawatemberere ndi pangʼono pomwe kapena kuwadalitsa!

Onani mutuwo Koperani




Numeri 23:25
3 Mawu Ofanana  

Taonani, anthuwo auka ngati mkango waukazi, nadzitukumula ngati mkango waumuna. Sugonanso kufikira utadya nyama yogwira, utamwa mwazi wa zophedwa.


Koma Balamu anayankha nati kwa Balaki, Sindinakuuzani ndi kuti, Chilichonse achinena Yehova, chomwecho ndizichita?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa